21 Itai nayankha mfumu nuti, Pali Yehova, pali mbuye wanga mfumu, zoonadi apo padzakhala mbuye wanga mfumu, kapena mpa imfa kapena mpa moyo, pomwepo padzakhalanso mnyamata wanu.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 15
Onani 2 Samueli 15:21 nkhani