2 Samueli 15:27 BL92

27 Ndipo mfumu inanenanso ndi Zadoki wansembeyo, Suli mlauli kodi? ubwere kumudzi mumtendere pamodzi ndi ana ako amuna awiri, Ahimaazi mwana wako ndi Jonatani mwana wa Abyatara.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 15

Onani 2 Samueli 15:27 nkhani