32 Ndipo kunali pakufika Davide ku mutu wa phiri, kumene amapembedza Mulungu, onani, Husai M-ariki anadzakomana naye ali ndi maraya ace ong'ambika, ndi dothi pamutu pace.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 15
Onani 2 Samueli 15:32 nkhani