36 Onani, ali nao komweko ana amuna ao awiri, Ahimaazi mwana wa Zadoki, ndi Jonatani mwana wa Abyatara; iwowa muwatumize kuti adzandiuze ciri conse mudzacimva.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 15
Onani 2 Samueli 15:36 nkhani