23 Ndipo Ahitofeli, pakuona kuti sautsata uphungu wace anamanga buru wace, nanyamuka, nanka kumudzi kwao, nakonza za pa banja lace, nadzipacika, nafa, naikidwa m'manda a atate wace.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 17
Onani 2 Samueli 17:23 nkhani