14 Pomwepo Yoabu anati, Sindiyenera kucedwa nawe. Natenga mikondo itatu nagwaza nayo mtima wa Abisalomu alikukhala wamoyo pakati pa mtengowo.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18
Onani 2 Samueli 18:14 nkhani