2 Samueli 18:14 BL92

14 Pomwepo Yoabu anati, Sindiyenera kucedwa nawe. Natenga mikondo itatu nagwaza nayo mtima wa Abisalomu alikukhala wamoyo pakati pa mtengowo.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18

Onani 2 Samueli 18:14 nkhani