2 Samueli 2:24 BL92

24 Koma Yoabu ndi Abisai anampitikitsa Abineri; ndipo dzuwa linawalowera pofika ku citunda ca Ama, cakuno ca Giya, pa njira ya ku cipululu ca Gibeoni.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 2

Onani 2 Samueli 2:24 nkhani