2 Samueli 22:1 BL92

1 Ndipo Davide analankhula kwa Yehova mau a nyimbo iyi tsikuli Yehova anampulumutsa m'dzanja la adani ace onse, ndi m'dzanja la Sauli.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 22

Onani 2 Samueli 22:1 nkhani