2 Samueli 3:7 BL92

7 Ndipo Sauli adali ndi mkazi wamng'ono, dzina lace ndiye Rizipa, mwana wa Aya. Ndipo Isiboseti anati kwa Abineri, Unalowana bwanji ndi mkazi wamng'ono wa atate wanga?

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 3

Onani 2 Samueli 3:7 nkhani