2 Samueli 6:21 BL92

21 Koma Davide ananena ndi Mikala, Ndatero pamaso pa Yehova, amene anandisankha ine ndi kupitirira atate wako ndi banja lace lonse, nandiika ndikhale mtsogoleri wa anthu a Yehova, wa Israyeli, cifukwa cace ndidzasewera pamaso pa Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 6

Onani 2 Samueli 6:21 nkhani