2 Samueli 7:10 BL92

10 Ndipo ndidzaikira anthu anga Israyeli malo, ndi kuwaoka kuti akakhale m'malo ao a iwo okha, osasunthikanso. Ndipo anthu a mphulupulu sadzawabvutanso, monga poyamba paja,

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 7

Onani 2 Samueli 7:10 nkhani