Aroma 16:25 BL92

25 Ndipo kwa iye amene ali wamphamvu yakukhazikitsa inu monga mwa uthenga wanga wabwino, ndi kulalildra kwa Yesu Kristu, monga mwa bvumbulutso la cinsinsi cimene cinabisika mwa nthawi zonse zosayamba,

Werengani mutu wathunthu Aroma 16

Onani Aroma 16:25 nkhani