Marko 10:1 BL92

1 Ndipo ananyamuka Iye kumeneko, nadza ku maiko a ku Yudeya ndi ku tsidya lija la Yordano; ndipo anasonkhananso kwa Iye makamu a anthu; ndipo monga anazolowera, anawaphunzitsanso.

Werengani mutu wathunthu Marko 10

Onani Marko 10:1 nkhani