Marko 9:50 BL92

50 Mcere uli wabwino; koma ngati mcere unasukuluka, mudzaukoleretsa ndi ciani? Khalani nao mcere mwa inu nokha, ndipo khalani ndi mtendere wina ndi mnzace.

Werengani mutu wathunthu Marko 9

Onani Marko 9:50 nkhani