2 Samueli 1:21 BL92

21 Mapiri inu a Giliboa,Pa inu pasakhale mame kapena mvula, kapena minda yakutengako zopereka.Pakuti kumeneko zikopa za amphamvu zinatayika koipa,Cikopa ca Sauli, monga ca wosadzozedwa ndi mafuta.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 1

Onani 2 Samueli 1:21 nkhani