2 Samueli 11:1 BL92

1 Ndipo kunali pofikanso caka, nyengo yakuturuka mafumu, Davide anatumiza Yoabu, pamodzi ndi anyamata ace, ndi Aisrayeli onse; ndipo iwo anasakaza ana a Amoni, naumangira misasa yankhondo Raba. Koma Davide anatsaliraku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 11

Onani 2 Samueli 11:1 nkhani