10 Ndipo Amnoni anati kwa Tamara, Bwera naco cakudya kucipinda kuti ndikadye ca m'manja mwako. Ndipo Tamara anatenga timitanda anatipangato, nabwera nato kucipinda kwa Amnoni mlongo wace.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13
Onani 2 Samueli 13:10 nkhani