9 Ndipo anatenga ciwaya natiturutsa pamaso pace; koma anakana kudya. Ndipo Amnoni anati, Anthu onse aturuke kundisiya ine. Naturuka onse, kumsiya.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13
Onani 2 Samueli 13:9 nkhani