18 Ndipo iye anabvala cobvala ca mawanga mawanga, popeza ana akazi a mfumu okhala anamwali amabvala zotere. Ndipo mnyamata wace anamturutsa, napiringidza citseko atapita iye.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13
Onani 2 Samueli 13:18 nkhani