25 Ndipo m'lsrayeli monse munalibe wina anthu anamtama kwambiri cifukwa ca kukongola kwace monga Abisalomu; kuyambira ku mapazi kufikira pakati pa mutu wace mwa iye munalibe cirema.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 14
Onani 2 Samueli 14:25 nkhani