4 Pomwepo mfumu inanena ndi Ziba, Ona, za Mefiboseti zonse ziri zako. Ndipo Ziba anati, Ndikulambirani, mundikomere mtima, mbuye wanga mfumu.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 16
Onani 2 Samueli 16:4 nkhani