2 Samueli 18:17 BL92

17 Ndipo anatenga Abisalomu namponya m'cidzenje cacikuru kunkhalangoko; naunjika pamwamba pace mulu waukuru ndithu wamiyala; ndipo Aisrayeli onse anathawa yense ku hema wace.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18

Onani 2 Samueli 18:17 nkhani