2 Samueli 18:4 BL92

4 Ndipo mfumu inanena nao, Ndidzacita cimene cikomera inu. Mfumu niima pambali pa cipata, ndipo anthu onse anaturuka ali mazana, ndi zikwi.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18

Onani 2 Samueli 18:4 nkhani