13 Ndipo munene ndi Amasa, Suli pfupa langa ndi mnofu wanga kodi? Mulungu andilange naonjezepo ngati sudzakhala cikhalire kazembe wa khamu la ankhondo pamaso panga, m'malo mwa Yoabu.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 19
Onani 2 Samueli 19:13 nkhani