32 Ndipo Barizilai anali nkhalamba, ndiye wa zaka makumi asanu ndi atatu; ndiye amene anapereka cakudya kwa mfumu muja anagona ku Mahanaimu, pakuti anali munthu womveka ndithu.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 19
Onani 2 Samueli 19:32 nkhani