2 Samueli 20:7 BL92

7 Ndipo anaturuka namtsata anthu a Yoabu, ndi Akereti ndi Apeleti, ndi anthu onseamphamvu; naturuka m'Yerusalemu kukalondola Seba mwana wa Bikri.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 20

Onani 2 Samueli 20:7 nkhani