2 Samueli 21:16 BL92

16 Ndipo Isibenobi, ndiye wa ana a Rafa, amene kulemera kwa mkondo wace kunali masekeli mazana atatu a mkuwa, iyeyo anabvala lupanga latsopano, nati aphe Davide.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 21

Onani 2 Samueli 21:16 nkhani