17 Koma Abisai mwana wa Zeruya anamthandiza namkantha Mfliistiyo, namupha. Pomwepo anthu a Davide anamlumbirira iye nati, Inu simudzaturuka nafenso kunkhondo, kuti mungazime nyali ya Israyeli.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 21
Onani 2 Samueli 21:17 nkhani