9 niwapereka m'manja a Agibeoni, iwo nawapacika m'phiri pamaso pa Yehova, ndipo anagwa pamodzi onse asanu ndi awiri; m'masiku a kukolola, m'masiku oyamba, poyamba kuceka barele.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 21
Onani 2 Samueli 21:9 nkhani