7 M'kusauka kwanga ndinaitana kwa Yehova,Inde ndinakuwira kwa Mulungu wanga;Ndipo Iye anamva mau anga ali m'kacisi wace,Ndi kulira kwanga kunafika ku makutuace.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 22
Onani 2 Samueli 22:7 nkhani