2 Samueli 23:19 BL92

19 Kodi iye sindiye waulemu mwa atatuwa? cifukwa cace anali kazembe wao; ngakhale iyenso sadafikana ndi atatu oyamba.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 23

Onani 2 Samueli 23:19 nkhani