1 Ndipo panali nkhondo nthawi yaitali pakati pa nyumba ya Sauli ndi nyumba ya Davide. Koma Davide analimba cilimbire, ndi nyumba ya Sauli inafoka cifokere.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 3
Onani 2 Samueli 3:1 nkhani