9 Ndipo ananena ndi ine, Lemba, Odala iwo amene aitanidwa ku phwando la ukwati wa Mwanawankhosa. Ndipo ananena ndi ine, Iwo ndiwo mau oona a Mulungu.
Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 19
Onani Cibvumbulutso 19:9 nkhani