Cibvumbulutso 20:6 BL92

6 Wodala ndi woyera mtima ali iye amene acita nao pa kuuka koyamba; pa iwowa imfa yaciwiri iribe ulamuliro; komatu adzakhala ansembe a Mulungu ndi a Kristu, nadzacita ufumu pamodzi ndi iye zaka cikwizo.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 20

Onani Cibvumbulutso 20:6 nkhani