5 Ndipo Iye wakukhala pa mpando wacifumu anati, Taonani, ndicita zonse zikhale zatsopano. Ndipo ananena, Talemba; pakuti mau awa ali okhulupirika ndi oona.
Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 21
Onani Cibvumbulutso 21:5 nkhani