Yohane 11:4 BL92

4 Koma Yesu pamene anamva, anati, Kudwala kumene sikuli kwa imfa, koma cifukwa ca ulemerero wa Mulungu, kuti Mwana wa Mulungu alemekezedwe nako.

Werengani mutu wathunthu Yohane 11

Onani Yohane 11:4 nkhani