Yohane 14:17 BL92

17 ndiye Mzimu wa coonadi; amene dziko lapansi silingathe kumlandira, pakuti silimuona iye, kapena kumzindikira iye. Inu mumzindikira iye; cifukwa akhala ndi inu nadzakhala mwa inu.

Werengani mutu wathunthu Yohane 14

Onani Yohane 14:17 nkhani