Yohane 19:41 BL92

41 Koma kunali munda kumalo kumene anapacikidwako, ndi m'mundamo munali manda atsopano m'mene sanaikidwamo munthu ali yense nthawi zonse.

Werengani mutu wathunthu Yohane 19

Onani Yohane 19:41 nkhani