Yohane 21:16 BL92

16 Ananena nayenso kaciwiri, Simoni mwana wa Yona, ukonda Ine kodi? Ananena ndi iye, Inde, Ambuye; mudziwa kuti ndikukondani Inu. Ananena naye, Weta nkhosa zanga.

Werengani mutu wathunthu Yohane 21

Onani Yohane 21:16 nkhani