Yohane 21:18 BL92

18 Indetu, indetu, ndinena ndi iwe, pamene unali mnyamata unadzimangira wekha m'cuuno, ndipo unayenda kumene unafuna; koma pamene udzakalamba udzaturutsa manja ako, ndipo adzakumanga wina, nadzakunyamula kumene sufuna.

Werengani mutu wathunthu Yohane 21

Onani Yohane 21:18 nkhani