1 Cifukwa cace pamene Ambuye anadziwa kuti Afarisi adamva kuti Yesu anayesa anthu ophunzira, nawabatiza koposa Yohane
2 (angakhale Yesu sanabatiza yekha koma ophunzira ace),
3 anacokera ku Yudeya, namukanso ku Galileya.
4 Ndipo anayenerakupita pakati pa Samariya.