Yohane 4:9 BL92

9 Pamenepo mkazi wa m'Samariya ananena ndi iye, Bwanji Inu, muli Myuda, mupempha kwa ine kumwa, ndine mkazi Msamariya? (pakuti Ayuda sayenderana nao Asamariya),

Werengani mutu wathunthu Yohane 4

Onani Yohane 4:9 nkhani