1 Zitapita izi panali phwando la Ayuda; ndipo Yesu anakwera kunka ku Yerusalemu.
2 Koma pali thamanda m'Yerusalemu pa cipata ca nkhosa, lochedwa m'Cihebri Betesda, liri ndi makumbi asanu.
3 M'menemo munagona khamu lalikuru la anthu odwala akhungu, opunduka miyendo, opuwala. [
4 ]