Yohane 6:22 BL92

22 M'mawa mwace khamu la anthu limene linaima tsidya lija la nyanja linaona kuti palibe ngalawa yina koma imodzi, ndi kuti Yesu sanalowa pamodzi ndi akuphunzira ace m'ngalawamo, koma akuphunzira ace adacoka pa okha;

Werengani mutu wathunthu Yohane 6

Onani Yohane 6:22 nkhani