Yohane 6:35 BL92

35 Yesu anati kwa iwo, Ine ndine mkate wamoyo; iye amene adza kwa Ine sadzamva njala, ndi iye amene akhulupirira Ine sadzamva ludzu nthawi zonse.

Werengani mutu wathunthu Yohane 6

Onani Yohane 6:35 nkhani