Yohane 7:28 BL92

28 Pamenepo Yesu anapfuula m'Kacisi, alikuphunzitsa ndi kunena, Mundidziwa Ine, ndiponso mudziwa uko ndicokera; ndipo sindinadza Ine ndekha, koma iye wondituma Ine amene inu simumdziwa, ali woona.

Werengani mutu wathunthu Yohane 7

Onani Yohane 7:28 nkhani