2 Samueli 13:24 BL92

24 Abisalomu nafika kwa mfumu nati, Onani, ine mnyamata, wanu ndiri nao osenga nkhosa; inu mfumu ndi anyamata anu mupite nane mnyamata wanu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13

Onani 2 Samueli 13:24 nkhani