29 Pamenepo Abisalomu anaitana Yoabu kuti akamtumize iye kwa mfumu; koma anakana kubwera kwa iye; ndipo anamuitananso nthawi yaciwiri, koma anakana kubwera.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 14
Onani 2 Samueli 14:29 nkhani