2 Samueli 17:10 BL92

10 Ndipo ngakhale ngwazi imene mtima wace ukunga mtima wa mkango idzasungunuka konse, pakuti Aisrayeli onse adziwa atate wanu kuti ndiye munthu wamphamvu, ndi iwo ali naye ndiwo ngwazi.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 17

Onani 2 Samueli 17:10 nkhani