2 Samueli 8:1 BL92

1 Ndipo m'tsogolo mwace Davide anakantha Afilisti, nawagonjetsa; Davide nalanda mudzi wa Metege Ama m'manja mwa Afilisti.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 8

Onani 2 Samueli 8:1 nkhani